Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 23:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 “Lankhula ndi Aisiraeli, ndipo uwauze kuti, ‘Mʼmwezi wa 7, pa tsiku loyamba la mweziwo, muzipuma pa ntchito zanu zonse. Limeneli ndi tsiku la chikumbutso, ndipo lipenga likalira+ muzisonkhana kuti mulambire Mulungu.

  • Levitiko 23:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “Tsiku la 10 mʼmwezi wa 7 umenewu, ndi Tsiku la Mwambo Wophimba Machimo.+ Muzichita msonkhano wopatulika ndipo muzisonyeza kuti mukudzimvera chisoni*+ chifukwa cha machimo anu ndipo muzipereka nsembe yowotcha pamoto kwa Yehova.

  • 1 Mafumu 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Amuna onse a mu Isiraeli anasonkhana kwa Mfumu Solomo pachikondwerero* mʼmwezi wa Etanimu,* womwe ndi mwezi wa 7.+

  • Ezara 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pofika mwezi wa 7,+ Aisiraeli omwe ankakhala mʼmizinda yawo anasonkhana limodzi mogwirizana ku Yerusalemu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena