Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kwa zaka 6, muzidzala mbewu mʼminda yanu nʼkukolola mbewuzo.+ 11 Koma chaka cha 7 musamaulime, muziusiya kuti ugonere. Osauka amene ali pakati panu azidya zimene zili mʼmundamo ndipo zimene iwo asiya, nyama zakutchire zidzadya. Muzichita zimenezi ndi munda wanu wa mpesa komanso wa maolivi.

  • Levitiko 25:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Koma mʼchaka cha 7 dzikolo lizidzasunga sabata lopuma pa zonse, sabata la Yehova. Musamadzadzale mbewu mʼminda yanu kapena kudulira mitengo yanu ya mpesa. 5 Musamadzakolole mbewu zomera zokha kuchokera pa mbewu zimene munakolola chaka chapita, ndipo musamadzakololenso mphesa za mʼmitengo yanu yosadulirayo. Chaka chimenecho dziko lizidzapuma pa zonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena