Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 14:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “‘Ngakhale amuna atatu awa: Nowa,+ Danieli+ ndi Yobu,+ akanakhala mʼdzikolo, iwo okhawo akanatha kupulumutsa miyoyo yawo chifukwa chokhala olungama,’+ akutero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”

  • Yakobo 5:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Abale, pa nkhani ya kumva zowawa+ ndi kuleza mtima,+ tengerani chitsanzo cha aneneri amene analankhula mʼdzina la Yehova.*+ 11 Monga mmene mukudziwira, anthu amene anapirira timawaona kuti ndi odala.*+ Munamva za kupirira kwa Yobu+ ndipo mukudziwa madalitso amene Yehova* anamupatsa.+ Mukuona nokha kuti Yehova* ndi wachikondi chachikulu komanso wachifundo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena