Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 40:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndi ndani amene anayezapo* mzimu wa Yehova,

      Ndipo ndi ndani amene angamulangize ngati mlangizi wake?+

      14 Kodi anafunsirapo nzeru kwa ndani kuti amuthandize kumvetsa zinthu?

      Ndi ndani amene amamuphunzitsa njira yachilungamo,

      Kapena kumuphunzitsa kuti adziwe zinthu,

      Kapenanso kumusonyeza njira yokhalira womvetsadi zinthu?+

  • Aroma 11:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 “Ndani akudziwa maganizo a Yehova,* kapena ndani angakhale mlangizi wake?”+

  • 1 Akorinto 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Nanga “ndani akudziwa maganizo a Yehova* kuti amulangize?”+ Koma ife tili ndi maganizo a Khristu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena