Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 12:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Nʼchifukwa chiyani unanyoza mawu a Yehova pochita zoipa pamaso pake? Unapha Uriya Muhiti ndi lupanga.+ Kenako unatenga mkazi wake kuti akhale mkazi wako+ utapha Uriyayo ndi lupanga la Aamoni.+

  • 2 Samueli 12:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iweyo unachita zimenezi mobisa,+ koma ine ndidzazichita masana Aisiraeli onse akuona.’”

  • Salimo 94:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, kodi anthu oipa adzapitiriza kusangalala mpaka liti?

      Adzapitiriza kukondwera mpaka liti?+

  • Salimo 94:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo amanena kuti: “Ya sakuona,+

      Ndipo Mulungu wa Yakobo sakudziwa zimene zikuchitika.”+

  • Miyambo 30:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zimene mkazi wachigololo amachita ndi izi:

      Iye amadya nʼkupukuta pakamwa pake

      Kenako amanena kuti, “Sindinachite cholakwa chilichonse.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena