Mateyu 27:1, 2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Mʼmawa kutacha, ansembe aakulu onse limodzi ndi akulu a anthu anakambirana nʼkugwirizana kuti aphe Yesu.+ 2 Ndipo atamumanga, anapita kukamupereka kwa Bwanamkubwa Pilato.+ Luka 23:10, 11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Komabe ansembe aakulu ndi alembi ankangonyamukanyamuka nʼkumamuneneza mwaukali. 11 Ndiyeno Herode limodzi ndi asilikali ake anamuchitira zachipongwe.+ Anamunyoza+ pomuveka chovala chokongola kwambiri, kenako anamutumizanso kwa Pilato. Chivumbulutso 19:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Ndiyeno ndinaona chilombo, mafumu a dziko lapansi ndi asilikali awo atasonkhana pamodzi kuti amenyane ndi amene anakwera pahatchi uja ndi gulu lake lankhondo.+
27 Mʼmawa kutacha, ansembe aakulu onse limodzi ndi akulu a anthu anakambirana nʼkugwirizana kuti aphe Yesu.+ 2 Ndipo atamumanga, anapita kukamupereka kwa Bwanamkubwa Pilato.+
10 Komabe ansembe aakulu ndi alembi ankangonyamukanyamuka nʼkumamuneneza mwaukali. 11 Ndiyeno Herode limodzi ndi asilikali ake anamuchitira zachipongwe.+ Anamunyoza+ pomuveka chovala chokongola kwambiri, kenako anamutumizanso kwa Pilato.
19 Ndiyeno ndinaona chilombo, mafumu a dziko lapansi ndi asilikali awo atasonkhana pamodzi kuti amenyane ndi amene anakwera pahatchi uja ndi gulu lake lankhondo.+