Salimo 30:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Chifukwa mkwiyo wa Mulungu sukhalitsa pa munthu,+Koma munthu amene wasangalala naye* amamukomera mtima kwa moyo wake wonse.+ Munthu akhoza kulira usiku, koma mʼmawa amafuula mosangalala.+ Salimo 100:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Chifukwa Yehova ndi wabwino.+Chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapo mpaka kalekale,Ndipo kukhulupirika kwake kudzakhalapo ku mibadwo yonse.+
5 Chifukwa mkwiyo wa Mulungu sukhalitsa pa munthu,+Koma munthu amene wasangalala naye* amamukomera mtima kwa moyo wake wonse.+ Munthu akhoza kulira usiku, koma mʼmawa amafuula mosangalala.+
5 Chifukwa Yehova ndi wabwino.+Chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapo mpaka kalekale,Ndipo kukhulupirika kwake kudzakhalapo ku mibadwo yonse.+