Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 40:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Masoka amene andizungulira ndi ambiri moti sindingathe kuwawerenga.+

      Zolakwa zanga ndi zochuluka moti sindikutha kuona kumene ndikulowera.+

      Zachuluka kwambiri kuposa tsitsi lakumutu kwanga,

      Ndipo ndataya mtima.

  • Aroma 7:23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 koma ndimaona lamulo lina mʼthupi* langa likumenyana ndi malamulo amʼmaganizo mwanga+ nʼkundichititsa kukhala kapolo wa lamulo la uchimo+ limene lili mʼthupi* langa. 24 Munthu womvetsa chisoni ine! Ndani adzandipulumutse ku thupi limene likundichititsa kuti ndifeli?

  • Agalatiya 5:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chifukwa zimene thupi limalakalaka zimalimbana ndi mzimu ndipo mzimu nawonso umalimbana ndi thupi. Zinthu ziwiri zimenezi zimatsutsana kuti musachite zinthu zimene mumafuna kuchita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena