Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 56:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu Mulungu, ine ndikuyenera kukwaniritsa zimene ndinakulonjezani.+

      Ndidzapereka kwa inu nsembe zoyamikira.+

  • Salimo 116:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova,

      Pamaso pa anthu ake onse.+

  • Mlaliki 5:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ukalonjeza kwa Mulungu usamachedwe kukwaniritsa lonjezo lako,+ chifukwa Mulungu sasangalala ndi anthu opusa.+ Uzikwaniritsa zinthu zimene walonjeza.+ 5 Ndi bwino kuti usalonjeze kusiyana ndi kulonjeza koma osakwaniritsa zimene walonjezazo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena