Deuteronomo 23:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Mukalonjeza kanthu kwa Yehova Mulungu wanu+ musamachedwe kukwaniritsa zimene mwalonjezazo.+ Chifukwa Yehova Mulungu wanu adzafuna ndithu kuti mukwaniritse zimene mwalonjezazo. Mukapanda kutero mudzakhala kuti mwachimwa.+ Salimo 76:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Chitani malonjezo anu kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse+Anthu onse amene amuzungulira abweretse mphatso zawo mwamantha.+ Mateyu 5:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Komanso munamva kuti anthu akale anauzidwa kuti: ‘Musamalumbire koma osachita,+ mʼmalomwake muzikwaniritsa zimene mwalonjeza kwa Yehova.’*+
21 Mukalonjeza kanthu kwa Yehova Mulungu wanu+ musamachedwe kukwaniritsa zimene mwalonjezazo.+ Chifukwa Yehova Mulungu wanu adzafuna ndithu kuti mukwaniritse zimene mwalonjezazo. Mukapanda kutero mudzakhala kuti mwachimwa.+
11 Chitani malonjezo anu kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse+Anthu onse amene amuzungulira abweretse mphatso zawo mwamantha.+
33 Komanso munamva kuti anthu akale anauzidwa kuti: ‘Musamalumbire koma osachita,+ mʼmalomwake muzikwaniritsa zimene mwalonjeza kwa Yehova.’*+