Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mdaniyo anati: ‘Ndiwathamangira nʼkuwapeza!

      Ndigawa chuma chawo mpaka nditakhutira!

      Ndisolola lupanga langa! Dzanja langa liwawononga!’+

      10 Mwapemerera mpweya wanu, ndipo nyanja yawamiza.+

      Amira mʼmadzi akuya ngati chitsulo cholemera.

  • 1 Samueli 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Musamalankhule modzikweza,

      Pakamwa panu pasatuluke mawu odzikuza,

      Chifukwa Yehova ndi Mulungu wodziwa zonse,+

      Ndipo zochita za anthu, iye amaziyeza molondola.

  • Ezekieli 28:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Iwe mwana wa munthu, uza mtsogoleri wa Turo kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti:

      “Chifukwa chakuti wadzikuza mumtima mwako,+ ukumanena kuti, ‘Ndine mulungu.

      Ndakhala pampando wachifumu wa mulungu pakatikati pa nyanja.’+

      Koma ndiwe munthu basi, osati mulungu,

      Ngakhale kuti mumtima mwako umadziona kuti ndiwe mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena