Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 18:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakati pa anthuwa, usankhepo amuna oyenerera,+ oopa Mulungu, okhulupirika, odana ndi kupeza phindu mwachinyengo.+ Amenewa uwaike kuti akhale atsogoleri a anthuwa, ndipo pakhale atsogoleri a magulu a anthu 1,000, atsogoleri a magulu a anthu 100, atsogoleri a magulu a anthu 50 ndi atsogoleri a magulu a anthu 10.+ 22 Pakakhala mlandu uliwonse atsogoleri amenewa aziweruza anthuwo. Mlandu ukakhala wovuta azibwera nawo kwa iwe,+ koma mlandu uliwonse waungʼono, aziweruza. Uwalole amunawa kuti azikuthandiza kuchita zimenezi, kuti udzichepetsere ntchito.+

  • Salimo 82:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 “Ine ndanena kuti, ‘Inu ndinu milungu,*+

      Nonsenu ndinu ana a Wamʼmwambamwamba.

  • Yohane 10:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yesu anawafunsa kuti: “Kodi mʼChilamulo chanu sanalembemo kuti, ‘Ine ndanena kuti: “Inu ndinu milungu”’?*+ 35 Ngati anthu amene anatsutsidwa ndi mawu a Mulungu omwe satha mphamvu, anawatchula kuti ‘milungu,’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena