Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndinkaonekera kwa Abulahamu, Isaki ndi Yakobo monga Mulungu Wamphamvuyonse.+ Koma za dzina langa lakuti Yehova,+ ine sindinadzidziwikitse kwa iwo.+

  • Salimo 68:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Imbirani Mulungu, muimbireni nyimbo zotamanda dzina lake.+

      Imbirani Iye amene akudutsa mʼchipululu.*

      Dzina lake ndi Ya.*+ Sangalalani pamaso pake.

  • Yesaya 42:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ine ndine Yehova. Dzina langa ndi limeneli.

      Sindipereka ulemerero wanga kwa wina aliyense

      Ndipo sindifuna kuti aliyense azitamanda zifaniziro zogoba mʼmalo mwa ine.+

  • Yesaya 54:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa Wokupanga Wamkulu+ ali ngati mwamuna* wako,+

      Dzina lake ndi Yehova wa magulu ankhondo akumwamba,

      Ndipo Woyera wa Isiraeli ndiye Wokuwombola.+

      Iye adzatchedwa Mulungu wa dziko lonse lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena