-
2 Samueli 7:12-15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Ukadzamwalira+ nʼkugona mʼmanda ndi makolo ako, ndidzachititsa kuti mbadwa* yako, mwana wako weniweni, akhale mfumu ndipo ndidzachititsa kuti ufumu wake ukhazikike.+ 13 Iye ndi amene adzamangire dzina langa nyumba,+ ndipo ndidzakhazikitsa mpando wake wachifumu mpaka kalekale.+ 14 Ine ndidzakhala bambo ake ndipo iye adzakhala mwana wanga.+ Akalakwitsa zinthu zina, ine ndidzamudzudzula ndi ndodo ya anthu ndi zikoti za ana a anthu.*+ 15 Ndipo chikondi changa chokhulupirika sichidzachoka pa iye ngati mmene ndinachichotsera pa Sauli,+ amene ndinamʼchotsa pamaso pako.
-
-
Salimo 132:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Yehova walumbira kwa Davide.
Ndithudi sadzalephera kukwaniritsa mawu ake akuti:
-