Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 8:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ndikayangʼana kumwamba, ntchito ya zala zanu,

      Mwezi ndi nyenyezi zimene munapanga,+

  • Yesaya 48:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Dzanja langa linayala maziko a dziko lapansi,+

      Ndipo dzanja langa lamanja linatambasula kumwamba.+

      Ndikaitana zinthu zimenezi, zimaimirira limodzi.

  • Aheberi 1:10-12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iye akunenanso kuti: “Ambuye, pachiyambipo munakhazikitsa maziko a dziko lapansi, ndipo kumwamba ndi ntchito ya manja anu. 11 Zinthu zimenezi zidzatha, koma inu mudzakhalapobe. Mofanana ndi chovala, zonsezi zidzatha. 12 Mudzapindapinda zinthu zimenezi ngati mkanjo komanso ngati chovala ndipo zidzasinthidwa. Koma inu simudzasintha, ndipo mudzakhalapo mpaka kalekale.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena