Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 14:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zikanakhala bwino mukanandibisa mʼManda,*+

      Mukanandibisa mpaka mkwiyo wanu utadutsa,

      Zikanakhala bwino mukanandiikira nthawi nʼkudzandikumbukira.+

      14 Munthu akafa, kodi angakhalenso ndi moyo?+

      Ndidzadikira masiku onse a ntchito yanga yokakamiza,

      Mpaka mpumulo wanga utafika.+

  • Machitidwe 13:34-37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ndipo mfundo yakuti iye anamuukitsa ndipo sangabwererenso kuthupi limene limavunda,* anaifotokoza chonchi: ‘Ine ndidzakusonyezani anthu inu chikondi chokhulupirika chimene ndinalonjeza Davide. Lonjezo limeneli ndi lodalirika.’+ 35 Ndipo salimo lina limanenanso kuti, ‘Simudzalola kuti thupi la wokhulupirika wanu livunde.’+ 36 Davide anachita chifuniro cha Mulungu pa nthawi ya mʼbadwo wake, anamwalira nʼkuikidwa mʼmanda a makolo ake ndipo thupi lake linavunda.+ 37 Koma amene Mulungu anamuukitsa uja thupi lake silinavunde.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena