Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 34:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ngakhale mikango yamphamvu* ingakhale ndi njala chifukwa chosowa chakudya.

      Koma anthu amene akufunafuna Yehova sadzasowa chilichonse chabwino.+

  • Yesaya 55:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Nʼchifukwa chiyani anthu inu mukuwononga ndalama polipirira zinthu zimene si chakudya,

      Ndipo nʼchifukwa chiyani mukuwononga ndalama* zimene mwapeza polipirira zinthu zimene nʼzosakhutitsa?

      Tcherani khutu kwa ine kuti mudye zabwino,+

      Ndipo mudzasangalala kwambiri ndi zakudya zabwino.*+

  • Luka 1:53
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 53 Wakhutitsa anthu anjala ndi zinthu zabwino+ koma amene anali ndi chuma wawathamangitsa chimanjamanja.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena