Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Odya bwino ayenera kugwira ganyu kuti apeze chakudya,

      Koma anjala alibenso njala.+

      Wosabereka wabereka ana 7,+

      Koma amene anali ndi ana aamuna ambiri, ali yekhayekha.*

  • Salimo 34:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ngakhale mikango yamphamvu* ingakhale ndi njala chifukwa chosowa chakudya.

      Koma anthu amene akufunafuna Yehova sadzasowa chilichonse chabwino.+

  • Salimo 107:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Chifukwa iye wathetsa ludzu la anthu aludzu

      Ndipo anthu anjala wawadyetsa zinthu zabwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena