Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Atamandidwe Yehova Mulungu wa Isiraeli,

      Atamandidwe mpaka kalekale.’”

      Ndiyeno anthu onse ananena kuti, “Ame!”* ndipo anatamanda Yehova.

  • 1 Mbiri 29:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako Davide anatamanda Yehova pamaso pa mpingo wonse kuti: “Mutamandidwe inu Yehova Mulungu wa Isiraeli atate wathu, kuyambira kalekale mpaka kalekale.

  • Salimo 106:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Atamandike Yehova, Mulungu wa Isiraeli,

      Mpaka kalekale.*+

      Ndipo anthu onse anene kuti, “Ame!”

      Tamandani Ya,*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena