Salimo 51:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 51 Ndikomereni mtima inu Mulungu, mogwirizana ndi chikondi chanu chokhulupirika.+ Fufutani zolakwa zanga mogwirizana ndi chifundo chanu chachikulu.+ Salimo 103:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Mofanana ndi bambo amene amasonyeza chifundo kwa ana ake,Yehova wasonyezanso chifundo kwa anthu amene amamuopa.+ Salimo 119:116 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 116 Inu Mulungu, ndithandizeni mogwirizana ndi zimene munalonjeza,*+Kuti ndikhalebe ndi moyo.Musalole kuti ndichite manyazi chifukwa cha chiyembekezo changa.*+ Danieli 9:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Inu Mulungu wanga, tcherani khutu lanu kuti mumve. Tsegulani maso anu kuti muone zimene zatichitikira komanso mmene mzinda wodziwika ndi dzina lanu wawonongekera. Ifeyo sitikukuchondererani chifukwa choti tachita zinthu zolungama ayi, koma chifukwa cha chifundo chanu chachikulu.+ Luka 1:50 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 50 Kumibadwomibadwo iye amachitira chifundo anthu amene amamuopa.+
51 Ndikomereni mtima inu Mulungu, mogwirizana ndi chikondi chanu chokhulupirika.+ Fufutani zolakwa zanga mogwirizana ndi chifundo chanu chachikulu.+
13 Mofanana ndi bambo amene amasonyeza chifundo kwa ana ake,Yehova wasonyezanso chifundo kwa anthu amene amamuopa.+
116 Inu Mulungu, ndithandizeni mogwirizana ndi zimene munalonjeza,*+Kuti ndikhalebe ndi moyo.Musalole kuti ndichite manyazi chifukwa cha chiyembekezo changa.*+
18 Inu Mulungu wanga, tcherani khutu lanu kuti mumve. Tsegulani maso anu kuti muone zimene zatichitikira komanso mmene mzinda wodziwika ndi dzina lanu wawonongekera. Ifeyo sitikukuchondererani chifukwa choti tachita zinthu zolungama ayi, koma chifukwa cha chifundo chanu chachikulu.+