Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 18:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kenako Eliya anayandikira anthu onsewo nʼkunena kuti: “Kodi mukayikakayika mpaka liti?+ Ngati Yehova ali Mulungu woona mʼtsatireni,+ koma ngati Mulungu woona ndi Baala tsatirani ameneyo.” Koma anthuwo sanamuyankhe chilichonse.

  • Chivumbulutso 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma chifukwa choti ndiwe wofunda, osati wotentha+ kapena wozizira,+ ndikulavula mʼkamwa mwanga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena