Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 1:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Hana anali wokhumudwa kwambiri ndipo anayamba kupemphera kwa Yehova+ uku akulira kwambiri. 11 Iye analonjeza kuti: “Inu Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, mukaona kuvutika kwa ine kapolo wanu nʼkundikumbukira ndiponso mukapanda kundiiwala ine kapolo wanu nʼkundipatsa mwana wamwamuna,+ ndidzamʼpereka kwa Yehova masiku onse a moyo wake ndipo lezala silidzadutsa mʼmutu mwake.”+

  • 2 Samueli 16:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako Davide anauza Abisai ndi atumiki ake onse kuti: “Ngati mwana wanga weniweni, wobereka ndekha akufunafuna moyo wanga,+ kuli bwanji munthu wa fuko la Benjaminiyu?+ Musiyeni anyoze, chifukwa Yehova ndi amene wamuuza. 12 Mwina Yehova aona mavuto anga,+ ndipo Yehova adzabwezeretsa zabwino kwa ine mʼmalo mwa zimene Simeyi akunena lero pondinyoza.”+

  • Yesaya 38:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Hezekiya mfumu ya Yuda atadwala nʼkuchira, analemba zotsatirazi.

  • Yesaya 38:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Inu Yehova, ndipulumutseni,

      Ndipo ine ndi anthu ena tidzaimba nyimbo zanga ndi zoimbira za zingwe+

      Kunyumba ya Yehova masiku onse a moyo wathu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena