Salimo 78:70 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 70 Anasankha Davide+ mtumiki wake,Ndipo anamuchotsa kumakola a nkhosa,+ Salimo 138:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ngakhale kuti Yehova ali pamwamba, amaona wodzichepetsa,+Koma wonyada samuyandikira.+
70 Anasankha Davide+ mtumiki wake,Ndipo anamuchotsa kumakola a nkhosa,+ Salimo 138:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ngakhale kuti Yehova ali pamwamba, amaona wodzichepetsa,+Koma wonyada samuyandikira.+