-
2 Mbiri 7:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Aisiraeli onse ankaonerera pamene moto unkatsika ndiponso pamene ulemerero wa Yehova unali pamwamba pa nyumbayo. Ataona zimenezi, anagwada nʼkuwerama mpaka nkhope zawo kufika pansi ndipo anayamika Yehova, “chifukwa iye ndi wabwino ndipo chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapo mpaka kalekale.”
-