Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Aisiraeli onse ankaonerera pamene moto unkatsika ndiponso pamene ulemerero wa Yehova unali pamwamba pa nyumbayo. Ataona zimenezi, anagwada nʼkuwerama mpaka nkhope zawo kufika pansi ndipo anayamika Yehova, “chifukwa iye ndi wabwino ndipo chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapo mpaka kalekale.”

  • 2 Mbiri 20:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Atakambirana ndi anthuwo, iye anasankha anthu oti aziimbira+ Yehova ndiponso kumutamanda atavala zovala zokongola ndi zopatulika ndipo ankayenda patsogolo pa amuna onyamula zida. Iwo ankanena kuti: “Yamikani Yehova, chifukwa chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapo mpaka kalekale.”+

  • Salimo 106:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 106 Tamandani Ya!*

      Yamikani Yehova chifukwa iye ndi wabwino.+

      Chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapo mpaka kalekale.+

  • Salimo 107:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 107 Yamikani Yehova, chifukwa iye ndi wabwino.+

      Chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapobe mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena