Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 52:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 52 Nʼchifukwa chiyani ukudzitukumula chifukwa cha zinthu zoipa zimene ukuchita, wamphamvu iwe?+

      Chikondi chokhulupirika cha Mulungu nʼchokhalitsa.+

       2 Lilime lako limene ndi lakuthwa ngati lezala,+

      Limakonza chiwembu komanso kuchita zachinyengo.+

  • Salimo 58:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Oipa amasochera* akangobadwa.*

      Iwo amakhala osamvera komanso abodza kuchokera nthawi imene anabadwa.

       4 Iwo ali ndi poizoni ngati wa njoka.+

      Ndipo ndi ogontha ngati njoka ya mamba imene yatseka makutu ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena