Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mlaliki 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Poti zonse zanenedwa, mfundo yaikulu ndi yakuti: Opa Mulungu woona+ ndi kusunga malamulo ake+ chifukwa zimenezi ndi zimene munthu akuyenera kuchita.+

  • Mika 6:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye anakuuza munthu iwe zimene zili zabwino.

      Kodi Yehova akufuna kuti uzichita* chiyani?

      Iye akungofuna kuti uzichita chilungamo,*+ uziona kuti kukhulupirika nʼkofunika,*+

      Ndiponso uziyenda modzichepetsa+ ndi Mulungu wako.+

  • Mateyu 22:37-40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Iye anamuyankha kuti: “‘Muzikonda Yehova* Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse, moyo wanu wonse ndi maganizo anu onse.’+ 38 Limeneli ndi lamulo lalikulu kwambiri komanso loyamba. 39 Lachiwiri lofanana nalo ndi ili: ‘Uzikonda mnzako mmene umadzikondera wekha.’+ 40 Chilamulo chonse chagona pa malamulo awiri amenewa, kuphatikizaponso zimene aneneri analemba.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena