Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 19:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Popeza kuti Yonatani, mwana wa Sauli, ankakonda kwambiri Davide,+ iye anauza Davide kuti: “Bambo anga akufuna kukupha. Chonde mawa mʼmawa usamale. Udzapite kukabisala ndipo ukakhale komweko.

  • 1 Samueli 19:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho Yonatani analankhula zabwino za Davide+ kwa Sauli bambo ake. Iye anawauza kuti: “Mfumu isachimwire mtumiki wake Davide, chifukwa iye sanakulakwireni, ndipo wakhala akukuchitirani zinthu zabwino kwambiri.

  • Miyambo 17:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mnzako weniweni amakusonyeza chikondi nthawi zonse,+

      Ndipo ndi mʼbale amene anabadwa kuti akuthandize pakagwa mavuto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena