Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 5:8-10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ukhale kutali kwambiri ndi iye.

      Usayandikire pakhomo la nyumba yake,+

       9 Kuti usapereke ulemu wako kwa anthu ena+

      Komanso kuti usakumane ndi mavuto mʼzaka zotsala za moyo wako.*+

      10 Ndiponso kuti alendo asakuwonongere zinthu zako,*+

      Komanso kuti zinthu zimene unazipeza movutikira zisapite kunyumba ya mlendo.

  • Miyambo 6:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Munthu amafika potsala ndi mkate umodzi wokha chifukwa cha hule,+

      Koma mkazi wa mwini amasaka moyo wako wamtengo wapatali.

  • Luka 15:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Patangopita masiku owerengeka, mwana wamngʼono uja anasonkhanitsa zinthu zake zonse nʼkupita kudziko lina lakutali. Kumeneko anayamba kukhala moyo wotayilira ndipo anasakaza chuma chake chonse. 14 Atawononga chuma chake chonse, mʼdziko lonselo munagwa njala yaikulu ndipo iye anayamba kuvutika kwambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena