Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 20:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Kukhulupirika komanso chikondi chokhulupirika zimateteza mfumu.+

      Mfumuyo ikamasonyeza chikondi chokhulupirika, mpando wake wachifumu umakhazikika.+

  • Miyambo 25:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chotsani woipa pamaso pa mfumu,

      Ndipo mpando wake wachifumu udzakhazikika chifukwa cha chilungamo.+

  • Yesaya 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ulamuliro* wake udzafika kutali

      Ndipo mtendere sudzatha,+

      Pampando wachifumu wa Davide+ ndiponso mu ufumu wake

      Kuti iye achititse ufumuwo kukhazikika+ ndiponso kukhala wolimba

      Pogwiritsa ntchito chilungamo+ ndiponso mtima wowongoka,+

      Kuyambira panopa mpaka kalekale.

      Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzachita zimenezi modzipereka kwambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena