Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Phunzitsa mwana kuti aziyenda mʼnjira imene akuyenera kuyendamo.+

      Ngakhale akadzakalamba sadzachoka mʼnjira imeneyo.+

  • Miyambo 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Uchitsiru umakhazikika mumtima mwa mwana.+

      Koma ndodo yomulangira ndi imene imauthamangitsira kutali ndi iye.+

  • Miyambo 23:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mwana usalephere kumupatsa chilango.*+

      Ngakhale utamukwapula ndi chikwapu, sangafe.

  • Aefeso 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Inu abambo, musamapsetse mtima ana anu,+ koma pitirizani kuwalera powapatsa malangizo*+ komanso kuwaphunzitsa mogwirizana ndi zimene Yehova* amanena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena