Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 1:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Komanso, Mulungu anawadalitsa nʼkuwauza kuti: “Muberekane, muchuluke, mudzaze dziko lapansi+ ndipo muziliyangʼanira.+ Muyangʼanirenso+ nsomba zamʼnyanja ndi zamoyo zouluka mumlengalenga, komanso chamoyo chilichonse choyenda padziko lapansi.”

  • Genesis 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mulungu anadalitsa Nowa ndi ana ake, nʼkuwauza kuti: “Muberekane, muchuluke ndipo mudzaze dziko lapansi.+

  • Salimo 37:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Olungama adzalandira dziko lapansi,+

      Ndipo adzakhala mmenemo mpaka kalekale.+

  • Salimo 115:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kunena za kumwamba, kumwamba ndi kwa Yehova,+

      Koma dziko lapansi analipereka kwa ana a anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena