Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 35:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Kumeneko kudzakhala msewu waukulu+

      Inde msewu umene udzatchedwe Msewu Wopatulika.

      Munthu wodetsedwa sadzayenda mumsewu umenewo.+

      Amene adzayendemo ndi munthu yekhayo amene ali woyenerera.

      Palibe munthu wopusa amene adzayende mumsewu umenewo.

  • Yesaya 60:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Anthu ako onse adzakhala olungama.

      Adzatenga dzikoli kukhala lawo mpaka kalekale.

      Anthuwo ndi mmera umene ndinadzala,

      Ndiponso ntchito ya manja anga,+ kuti ineyo ndioneke kukongola.+

  • Chivumbulutso 21:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Koma chilichonse chodetsedwa komanso aliyense wochita zonyansa ndiponso zachinyengo, sadzalowa mumzindawo.+ Amene adzalowemo ndi okhawo amene mayina awo analembedwa mumpukutu wa moyo wa Mwanawankhosa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena