Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 48:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 ‘Muledzeretseni+ chifukwa wadzikuza pamaso pa Yehova.+

      Mowabu akugubuduka mʼmasanzi ake,

      Ndipo wakhala chinthu choyenera kuchinyoza.

  • Yeremiya 48:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 “Tamva za kunyada kwa Mowabu. Iye ndi wodzikuza kwambiri.

      Tamva za kudzitukumula kwake, kunyada kwake, kudzikweza kwake ndi kudzikuza kwa mtima wake.”+

  • Zefaniya 2:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli wanena kuti: “Pali ine Mulungu wamoyo,

      Mowabu adzakhala ngati Sodomu,+

      Ndipo Amoni adzakhala ngati Gomora,+

      Malo okhala ndi zomera zoyabwa, dothi lamchere ndiponso malo abwinja mpaka kalekale.+

      Anthu anga amene adzatsale adzatenga zinthu za anthu amenewa,

      Ndipo anthu amtundu wanga amene adzatsale, adzawalanda anthuwa zinthu zawo.

      10 Anthu amenewo adzaona zimenezi chifukwa cha kunyada kwawo,+

      Chifukwa ankanyoza anthu a Yehova wa magulu ankhondo akumwamba ndipo ankadzikweza pamaso pawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena