-
2 Mafumu 10:32, 33Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
32 Mʼmasiku amenewo, Yehova anayamba kuchepetsa dziko la Isiraeli pangʼono ndi pangʼono. Ndipo Hazaeli anapitiriza kuukira Aisiraeli mʼmadera awo onse.+ 33 Anayambira kumʼmawa kwa Yorodano, ku Giliyadi konse, dera lonse la Gadi, la Rubeni ndi la Manase,+ kuyambira ku Aroweli yemwe ali pafupi ndi chigwa* cha Arinoni mpaka ku Giliyadi ndi Basana.+
-