Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mʼchaka cha 9 cha Hoshiya, mfumu ya Asuri inalanda Samariya+ nʼkutenga Aisiraeli kupita nawo ku Asuri.+ Mfumuyo inakaika Aisiraeliwo ku Hala ndi ku Habori pafupi ndi mtsinje wa Gozani+ ndiponso mʼmizinda ya Amedi.+

  • Yesaya 7:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Chifukwa likulu la Siriya ndi Damasiko,

      Ndipo mfumu ya Damasiko ndi Rezini.

      Zaka 65 zisanathe,

      Efuraimu adzakhala ataphwanyidwaphwanyidwa ndipo sadzakhalanso mtundu wa anthu.+

  • Yesaya 28:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsoka kwa chisoti* chokongola* cha zidakwa za ku Efuraimu+

      Komanso maluwa ake okongola amene akufota!

      Maluwawo avalidwa ndi mzinda umene uli paphiri, pamwamba pa chigwa chachonde, kumene zidakwa zoledzera ndi vinyozo zimakhala.

       2 Taonani! Yehova ali ndi winawake wamphamvu komanso wanyonga.

      Mofanana ndi mvula yamabingu komanso yamatalala, mvula yamphepo yowononga,

      Mofanana ndi mvula yamabingu ya madzi amphamvu osefukira,

      Iye adzagwetsera pansi chisoti chaulemererocho mwamphamvu.

  • Hoseya 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ine ndidzakhala ngati mkango wamphamvu kwa Efuraimu,

      Ndiponso ngati mkango wamphamvu kwa anthu a mʼnyumba ya Yuda.

      Ineyo ndidzawakhadzulakhadzula nʼkuchoka.+

      Ndidzawatenga nʼkukawataya ndipo palibe adzawalanditse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena