-
Yesaya 6:11, 12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Atatero ndinafunsa kuti: “Mpaka liti, inu Yehova?” Iye anayankha kuti:
-
-
Maliro 2:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Iye wameza nsanja zonse za Isiraeli.
Wawononga malo ake onse okhala ndi mipanda yolimba kwambiri.
Ndipo wachititsa kuti paliponse pakhale maliro komanso kulira mumzinda wa mwana wamkazi wa Yuda.
-
-
Ezekieli 36:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Choncho inu mapiri a ku Isiraeli, imvani mawu a Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa. Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wauza mapiri ndi zitunda, mitsinje ndi zigwa, mabwinja a malo amene anawonongedwa+ komanso mizinda yopanda anthu imene anthu a mitundu ina amene anapulumuka anaitenga kuti ikhale yawo. Anthuwo ankakhala moizungulira ndipo ankainyoza.+
-