Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 36:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova Mulungu wa makolo awo anapitiriza kuwachenjeza kudzera mwa atumiki ake. Ankawachenjeza mobwerezabwereza chifukwa ankamvera chisoni anthu akewo ndiponso malo ake okhala. 16 Koma iwo anapitiriza kunyoza atumiki a Mulungu woona,+ kunyoza mawu ake+ ndiponso kuseka aneneri ake.+ Iwo anafika poti panalibenso chiyembekezo choti angathe kuchiritsidwa. Kenako Yehova anawakwiyira kwambiri nʼkuwalanga.+

  • Yesaya 8:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iye adzakhala ngati malo opatulika,

      Koma kwa nyumba zonse ziwiri za Isiraeli,

      Adzakhala ngati mwala wopunthwitsa+

      Ndiponso ngati thanthwe lokhumudwitsa.

      Adzakhala ngati msampha komanso khwekhwe

      Kwa anthu okhala mu Yerusalemu.

      15 Anthu ambiri pakati pawo adzapunthwa nʼkugwa ndipo adzathyoka.

      Iwo adzakodwa nʼkugwidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena