Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 46:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kutatsala nthawi yaitali, ndimaneneratu zimene zidzachitike,

      Ndipo kale kwambiri ndinaneneratu zinthu zimene zidzachitike mʼtsogolo.+

      Ine ndimanena kuti, ‘Zolinga zanga zidzachitikadi,+

      Ndipo ndidzachita chilichonse chimene ndikufuna.’+

  • 1 Petulo 1:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pakuti “anthu onse ali ngati udzu, ndipo ulemerero wawo wonse uli ngati duwa lakutchire. Udzu umafota ndipo duwa limathothoka, 25 koma mawu a Yehova* adzakhalapo mpaka kalekale.”+ “Mawu” amenewa ndi uthenga wabwino umene unalengezedwa kwa inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena