Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 40:6-8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Tamvera! Winawake akunena kuti: “Lengeza mofuula!”

      Wina akufunsa kuti: “Ndilengeze mofuula za chiyani?”

      “Anthu onse ali ngati udzu wobiriwira.

      Chikondi chawo chonse chokhulupirika chili ngati duwa lakutchire.+

       7 Udzu wobiriwirawo umauma

      Ndipo maluwawo amafota,+

      Chifukwa mpweya* wa Yehova umauzira zinthu zimenezi.+

      Ndithu anthu ali ngati udzu wobiriwira.

       8 Udzu wobiriwira umauma,

      Maluwa amafota,

      Koma mawu a Mulungu wathu adzakhalapo mpaka kalekale.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena