Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 16:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Chifukwa minda yamʼmapiri ya ku Hesiboni+ yafota,

      Chimodzimodzinso mitengo ya mpesa ya ku Sibima,+

      Olamulira anthu a mitundu ina apondaponda nthambi zake zofiira kwambiri.*

      Nthambizo zinafika mpaka ku Yazeri,+

      Zinafika mpaka kuchipululu.

      Mphukira zake zinakula mpaka zinafika kunyanja.

       9 Nʼchifukwa chake ndidzalirire mtengo wa mpesa wa ku Sibima pamene ndikulirira Yazeri.

      Ndidzakunyowetsa kwambiri ndi misozi yanga iwe Hesiboni ndi Eleyale,+

      Chifukwa chakuti kufuula kosangalalira zipatso zamʼchilimwe komanso zokolola zako kwatha.*

  • Yeremiya 48:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Wowononga adzalowa mumzinda uliwonse,

      Ndipo sipadzapezeka mzinda wopulumuka.+

      Chigwa chidzawonongedwa,

      Chimodzimodzinso malo afulati,* mogwirizana ndi zimene Yehova wanena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena