-
Yeremiya 10:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Nʼchifukwa chake sanachite zinthu mozindikira,
Ndipo ziweto zawo zonse zabalalika.”+
-
-
Ezekieli 34:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Nkhosa zanga zinasochera mʼmapiri onse ndi mʼzitunda zonse zitalizitali. Nkhosa zanga zinabalalika padziko lonse lapansi ndipo panalibe amene ankazifufuza kapena kuziyangʼanayangʼana.
-