Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 10:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Abusa achita zinthu mopanda nzeru,+

      Ndipo sanafunse malangizo kwa Yehova.+

      Nʼchifukwa chake sanachite zinthu mozindikira,

      Ndipo ziweto zawo zonse zabalalika.”+

  • Yeremiya 23:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho Yehova Mulungu wa Isiraeli wadzudzula abusa amene akuweta anthu ake kuti: “Inu mwabalalitsa nkhosa zanga. Munapitiriza kuzimwaza ndipo simunazisamalire.”+

      “Tsopano ndikulangani chifukwa cha zochita zanu zoipa,” akutero Yehova.

  • Ezekieli 34:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Iwe mwana wa munthu, losera zoipa zimene zidzachitikire abusa a Isiraeli. Losera ndipo uuze abusawo kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Tsoka abusa a Isiraeli,+ amene akhala akungodzidyetsa okha! Kodi abusa ntchito yawo si kudyetsa nkhosa?+

  • Ezekieli 34:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Nkhosa zanga zinasochera mʼmapiri onse ndi mʼzitunda zonse zitalizitali. Nkhosa zanga zinabalalika padziko lonse lapansi ndipo panalibe amene ankazifufuza kapena kuziyangʼanayangʼana.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena