Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 23:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Tsoka abusa amene akuwononga ndi kubalalitsa nkhosa zapamalo anga odyetsera ziweto!” akutero Yehova.+

  • Ezekieli 34:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho zinamwazikana chifukwa zinalibe mʼbusa+ ndipo zinakhala chakudya cha zilombo zonse zakutchire. 6 Nkhosa zanga zinasochera mʼmapiri onse ndi mʼzitunda zonse zitalizitali. Nkhosa zanga zinabalalika padziko lonse lapansi ndipo panalibe amene ankazifufuza kapena kuziyangʼanayangʼana.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena