Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 48:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ayi, inu simunamve+ kapena kudziwa zimenezi,

      Ndipo mʼmbuyomu makutu anu anali osatseguka,

      Chifukwa ndikudziwa kuti inu ndi achinyengo,+

      Ndipo kuyambira pamene munabadwa mumatchedwa wochimwa.+

  • Yeremiya 3:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 ‘Ndithudi, mofanana ndi mkazi amene amasiya mwamuna wake mwachinyengo, inunso a mʼnyumba ya Isiraeli mwandichitira zachinyengo,’+ akutero Yehova.”

  • Hoseya 5:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Akhala osakhulupirika kwa Yehova,+

      Chifukwa abereka ana achilendo.

      Tsopano mwezi udzawadya* limodzi ndi zinthu zawo.*

  • Hoseya 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Koma iwo, mofanana ndi anthu wamba, aphwanya pangano.+

      Kumeneko andichitira zosakhulupirika.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena