Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 21:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Manase anaphanso anthu ambiri osalakwa mpaka magazi awo anadzaza Yerusalemu kuyambira koyambirira mpaka kumapeto,+ kuwonjezera pa tchimo lake lochititsa kuti Ayuda achimwe pochita zoipa pamaso pa Yehova.

  • Yesaya 59:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mapazi awo amathamangira kukachita zoipa,

      Ndipo amafulumira kukhetsa magazi a anthu osalakwa.+

      Maganizo awo ndi maganizo oipa.

      Zonse zimene amachita zimakhala zowononga ndiponso zobweretsa mavuto.+

  • Yeremiya 2:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ngakhale zovala zako zathimbirira ndi magazi a anthu osauka omwe ndi osalakwa,+

      Ngakhale kuti anthuwo sindinawapeze akuthyola nyumba kuti abe,

      Ndaona kuti magazi awo ali pazovala zako zonse.+

  • Maliro 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zimenezi zinachitika chifukwa cha machimo a aneneri ake ndi zolakwa za ansembe ake,+

      Amene anakhetsa magazi a anthu olungama mumzindawo.+

  • Mateyu 23:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Pa chifukwa chimenechi, ndikukutumizirani aneneri,+ anthu anzeru ndi aphunzitsi.+ Ena a iwo mudzawapha+ nʼkuwapachika pamtengo ndipo ena mudzawakwapula+ mʼmasunagoge mwanu ndi kuwazunza+ mumzinda ndi mzinda, 35 kuti magazi onse a anthu olungama amene anakhetsedwa padziko lapansi abwere pa inu. Kuyambira magazi a Abele wolungama+ mpaka magazi a Zekariya mwana wa Barakiya, amene inu munamupha pakati pa nyumba yopatulika ndi guwa lansembe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena