Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ulamuliro* wake udzafika kutali

      Ndipo mtendere sudzatha,+

      Pampando wachifumu wa Davide+ ndiponso mu ufumu wake

      Kuti iye achititse ufumuwo kukhazikika+ ndiponso kukhala wolimba

      Pogwiritsa ntchito chilungamo+ ndiponso mtima wowongoka,+

      Kuyambira panopa mpaka kalekale.

      Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzachita zimenezi modzipereka kwambiri.

  • Yesaya 11:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye adzasangalala ndi kuopa Yehova.+

      Sadzaweruza potengera zimene wangoona ndi maso ake,

      Kapena kudzudzula potengera zimene wangomva ndi makutu ake.+

       4 Adzaweruza mwachilungamo anthu onyozeka,

      Ndipo adzadzudzula anthu mowongoka mtima, pothandiza ofatsa apadziko lapansi.

      Adzakwapula dziko lapansi ndi ndodo ya pakamwa pake+

      Ndipo adzapha anthu oipa pogwiritsa ntchito mpweya* wamʼkamwa mwake.+

  • Yesaya 32:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Taonani! Mfumu+ idzalamulira mwachilungamo,+

      Ndipo akalonga adzalamuliranso mwachilungamo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena