Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako ndinanena kuti: “Mayo ine Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa! Kunena zoona, mwapusitsa kwambiri anthu awa+ ndiponso Yerusalemu ponena kuti, ‘Mudzakhala pa mtendere,’+ pamene lupanga lili pakhosi pathu.”*

  • Yeremiya 6:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Chifukwa aliyense kuyambira wamngʼono mpaka wamkulu, akupeza phindu mwachinyengo.+

      Kuyambira mneneri mpaka wansembe, aliyense akuchita zachinyengo.+

      14 Iwo akuyesa kuchiritsa mwachinyengo kuwonongeka kwa anthu anga* ponena kuti,

      ‘Kuli mtendere! Kuli mtendere!’

      Pamene kulibe mtendere.+

  • Yeremiya 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo akuyesa kuchiritsa mwachinyengo kuwonongeka kwa mwana wamkazi* wa anthu anga ponena kuti,

      ‘Kuli mtendere! Kuli mtendere!’

      Pamene kulibe mtendere.+

  • Ezekieli 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Zonsezi zidzachitika chifukwa chakuti iwo asocheretsa anthu anga ponena kuti, “Tili pa mtendere!” koma palibe mtendere.+ Munthu akamanga khoma lachipinda losalimba, iwo akumalipaka laimu.’*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena