Yesaya 47:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ine ndinakwiyira anthu anga.+ Ndinalola kuti cholowa changa chidetsedwe+Ndipo ndinawapereka mʼmanja mwako.+ Koma iwe sunawachitire chifundo.+ Ngakhale munthu wokalamba unamusenzetsa goli lolemera kwambiri.+ Yeremiya 6:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndadzazidwa ndi mkwiyo wa Yehova,Ndipo ndatopa ndi kuusunga.”+ “Tsanulirani mkwiyowo pa mwana amene ali mumsewu,+Pa gulu la anyamata amene asonkhana pamodzi. Onse adzagwidwa, mwamuna limodzi ndi mkazi wake,Anthu achikulire limodzi ndi anthu okalamba.+ Maliro 4:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Yehova wawabalalitsa+Ndipo sadzawakomeranso mtima. Anthu sadzalemekezanso ansembe+ kapena kuchitira chifundo amuna achikulire.”+
6 Ine ndinakwiyira anthu anga.+ Ndinalola kuti cholowa changa chidetsedwe+Ndipo ndinawapereka mʼmanja mwako.+ Koma iwe sunawachitire chifundo.+ Ngakhale munthu wokalamba unamusenzetsa goli lolemera kwambiri.+
11 Ndadzazidwa ndi mkwiyo wa Yehova,Ndipo ndatopa ndi kuusunga.”+ “Tsanulirani mkwiyowo pa mwana amene ali mumsewu,+Pa gulu la anyamata amene asonkhana pamodzi. Onse adzagwidwa, mwamuna limodzi ndi mkazi wake,Anthu achikulire limodzi ndi anthu okalamba.+
16 Yehova wawabalalitsa+Ndipo sadzawakomeranso mtima. Anthu sadzalemekezanso ansembe+ kapena kuchitira chifundo amuna achikulire.”+