Yesaya 54:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Usachite mantha,+ chifukwa sudzachititsidwa manyazi.+Usachite manyazi, chifukwa sudzakhumudwitsidwa. Iwe udzaiwala manyazi apaubwana wako,Ndipo sudzakumbukiranso kunyozeka kwa paumasiye wako. Yesaya 60:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ana a anthu amene ankakupondereza adzabwera nʼkudzagwada pamaso pako.Anthu onse amene ankakuchitira zachipongwe adzagwada pamapazi ako,Ndipo adzakutchula kuti mzinda wa Yehova,Ziyoni wa Woyera wa Isiraeli.+ Mika 7:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Iwe mdani* wanga, usasangalale chifukwa cha zimene zandichitikira. Ngakhale kuti ndagwa, ndidzadzuka.Ngakhale kuti ndili mumdima, Yehova adzakhala kuwala kwanga. Zefaniya 2:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 “Ndamva kunyoza kwa Mowabu+ ndi mawu achipongwe a Aamoni,+Amene ankanenera anthu anga nʼkumadzitama kuti alanda dziko lawo.”+ Zefaniya 3:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Pa nthawiyo ndidzalanga onse amene akukupondereza,+Ndipo ndidzapulumutsa wotsimphina.+Ndidzasonkhanitsa anthu amene anabalalitsidwa.+ Ndidzachititsa kuti akhale otchuka* komanso azitamandidwa,Mʼdziko lonse limene anachititsidwa manyazi.
4 Usachite mantha,+ chifukwa sudzachititsidwa manyazi.+Usachite manyazi, chifukwa sudzakhumudwitsidwa. Iwe udzaiwala manyazi apaubwana wako,Ndipo sudzakumbukiranso kunyozeka kwa paumasiye wako.
14 Ana a anthu amene ankakupondereza adzabwera nʼkudzagwada pamaso pako.Anthu onse amene ankakuchitira zachipongwe adzagwada pamapazi ako,Ndipo adzakutchula kuti mzinda wa Yehova,Ziyoni wa Woyera wa Isiraeli.+
8 Iwe mdani* wanga, usasangalale chifukwa cha zimene zandichitikira. Ngakhale kuti ndagwa, ndidzadzuka.Ngakhale kuti ndili mumdima, Yehova adzakhala kuwala kwanga.
8 “Ndamva kunyoza kwa Mowabu+ ndi mawu achipongwe a Aamoni,+Amene ankanenera anthu anga nʼkumadzitama kuti alanda dziko lawo.”+
19 Pa nthawiyo ndidzalanga onse amene akukupondereza,+Ndipo ndidzapulumutsa wotsimphina.+Ndidzasonkhanitsa anthu amene anabalalitsidwa.+ Ndidzachititsa kuti akhale otchuka* komanso azitamandidwa,Mʼdziko lonse limene anachititsidwa manyazi.