Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 19:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiyeno Yesaya mwana wa Amozi anatumiza uthenga kwa Hezekiya, wakuti: “Yehova Mulungu wa Isiraeli wanena kuti, ‘Ndamva pemphero lako+ lokhudza Senakeribu mfumu ya Asuri.+

  • 2 Mafumu 19:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Chifukwa kundipsera mtima kwako+ ndi kufuula kwako zafika mʼmakutu mwanga.+

      Ndidzakola mphuno yako ndi ngowe yanga ndipo ndidzamanga zingwe zanga+ pakamwa pako.

      Kenako ndidzakukoka nʼkukubweza kudzera njira imene unadutsa pobwera.”+

  • Ezekieli 29:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Umuuze kuti: ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti:

      “Ine ndikulanga iwe Farao mfumu ya Iguputo,+

      Iwe chilombo chachikulu chamʼnyanja chimene chagona mʼngalande zotuluka mumtsinje wake wa Nailo,+

      Ndipo wanena kuti, ‘Mtsinje wa Nailo ndi wanga.

      Ineyo ndinaupanga ndekha.’+

       4 Koma ine ndidzakukola ndi ngowe munsagwada zako nʼkuchititsa kuti nsomba zamʼngalande za mtsinje wa Nailo zikakamire kumamba ako.

      Ndidzakutulutsa mumtsinje wako wa Nailo pamodzi ndi nsomba zonse zamumtsinje wa Nailo zimene zakakamira kumamba ako.

  • Ezekieli 39:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndidzakubweza nʼkukutsogolera kuti uchoke kumadera akutali kwambiri akumpoto+ ndipo ndidzakubweretsa kumapiri a ku Isiraeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena