Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pakati pa motowo panali zinazake zooneka ngati angelo 4,*+ ndipo mngelo aliyense ankaoneka ngati munthu.

  • Ezekieli 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mapazi a angelowo anali owongoka ndipo anali ooneka ngati mapazi a mwana wa ngʼombe. Mapaziwo ankawala ngati kopa wopukutidwa bwino.+

  • Danieli 10:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 ndinaona munthu atavala nsalu+ ndipo mʼchiuno mwake anali atamangamo lamba wa golide wa ku Ufazi. 6 Thupi lake linkanyezimira ngati mwala wa kulusolito,+ nkhope yake inkawala ngati mphezi, maso ake ankaoneka ngati miyuni yamoto, manja ake komanso mapazi ake ankaoneka ngati kopa*+ wonyezimira, ndipo mawu ake ankamveka ngati mawu a gulu lalikulu la anthu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena